Mphate CCAP
Spreading the Gospel of Our Lord Jesus Christ..
Youth Comedy
Kubwererako m'mbuyo pang'ono
12.04.2026
31.05.2026
Chichewa Service
31.05.2026
Nthawi ya kuwerenga Mau
2 Samuel 6:12-23 (Akwerra Nalo Likasalo Kuliika ku Yerusalemu).
Mateyu 18:5-7 (Wamkulu Mu Ufumu wa Kumwamba).
29/05/2026
PA Beteli sizinatiphonye....
Ladies & Gentlemen a very big hand for Wisdom Chimbe
🎓 Bachelor of science in Environmental Science with Credit.
26/05/2026
26.05.2026
Tiyeni tiwerenge mwachidwi. 👇👇👇
25/05/2026
25.05.2026
📢📢📢ANNOUNCEMENT❗❗
Potengera mkumano omwe unalipo dzulo kwa onse omwe anali a Mphate Zone C, agwirizana kuti Zone yi igawidwe ndi maina a C komanso D.
Choncho tili ndi Mphate C imene ndi kuyambira pa Kasinje Turn Off, kudutsa M1 kufika pa Shop Ya Mtsitsa kutsetsereka mbali mwa mpanda wa Kings Foundation mpaka kwa Mr Dausi kukathera kwa Bambo Mjehani imeneyo ndiye Mphate C.
Kuchoka Kings Foundation mpaka ku Nkhande, Mbali inayi kukafika kwa chinyamula imeneyo ndiye Mphate D.
Inu muli mbali ti? Yenseyutu ndi Mphate CCAP, osasokoneza🤝🤝🤝
Omwe alalikira lero ndi Bambo Maxwell Josinto akulu a mpingo opuma a Mphate C.
Ndipo atamaliza kulalikira uthenga omwe mutu wake akuti "Kodi Timakhulupilira kuti Tidzalangidwa?"
Inunso mukhoza kudziyankhira panokha, anafunsa izi poyerekeza nkhani ya "Nowa".
Utatha ulaliki Abusa a mpingo wu Rev. Ndalakwanji adalitsanso Uniform ya Mvano Choir pa Mpingowu.
24May2026
Pakali pano tili mgawo la kuwerengedwa kwa Mau.
Ndipo kuwerenga koyamba ku kuchokera m'buku la Genesis 6:1-22_ "Kulowerera kwa mtundu wa anthu."
Kuwerenga kwa chiwiri Chipangano Chatsopano Mateyu 24:36-44_"Awachenjeza adikire."
24/05/2026
24May2026
📢📢📢 ANNOUNCEMENT!!!
MPHATE CCAP ZONE C, yagawidwa pawiri ndipo Ina ndi idzitchedwa C1 komanso Ina C2.
Tiyeni tonse amene tinali Mu zone yi lero tifike ku mlaga, tikadziwe Zone yomwe tili.
Ambuye akudalitseni.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Website
Address
Ntcheu