Odalitsika
MACHILITSO NDI MAU AMULUNGU
15/10/2025
RIP MULUNGU ATITHANDIZILE KUVETSETSA
Zatsimikizika tsopano kuti a-Malawi okwana khumi, asanu ndi atatu (18) ndi omwe afa pa ngozi ya bus yomwe inachitika ku Limpopo, m'dziko la South Africa.
Bus-yi inanyumala anthu opitilira 90 pa nthawi yomwe ngoziyi imachitika lamulungu lapitali.
Malingana ndi kalata yaku ofesi ya mtsogoleri wa dziko lino ndi nduna, nzika za dziko lino zokwana 18 zafa pa ngoziyo.
Kudzera mu kalatayo, mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika komanso mai wa fuko la dziko lino Getrude Mutharika, apepesa mawanja ofeledwa.
Pakadali pano, Mutharika wathokoza dziko la South Africa kaamba ka thandizo lomwe lapereka kwa okhudwa pa ngoziyo.
Mukalatayo, yomwe wasayinira ndi Justin Saidi, mlembi wamkulu mu ofesiyo, boma lati ndilodzipereka kupereka thandizo kwa mawanja omwe akhudzidwa ndi ngoziyo.
15/10/2025
Unduna woona za ubale wadziko lino ndi maiko ena watsimikiza kuti a Malawi 22 anali mu bus yomwe inachita ngozi ndikupha anthu oposela 40 Lamulungu usiku mu dera la Limpopo, ku South Africa.
Mu kalata yomwe yatuluka Lachiwiri usiku, undunawu wati wazindikira a Malawi 14 pomwe ena asanu ndi atatu akusowabe. Mwa omwe awazindikilawa, 8 akanali mu chipatala pomwe 6 awatulutsa.
Nyumba yofalitsa mawu ya BBC inalengeza lolemba kuti athu 42 afa pa ngozi ya bus m'mapiri ena pa msewu wa N1 mchigawo cha Limpopo. Bus-yo inali pa ulendo wobwera ku Malawi kudzera ku Zimbabwe, ndipo inanyamula nzika za Malawi ndi Zimbabwe.
Koma unduna-wu mu kalata yake wati anthu 43 ndiwo afa pangoziyo ndipo kuti bus-yo inanyamula anthu oposela 90. Undunawu sunapeze uthenga wa m'Malawi amene wamwalira pangoziyo koma wati akulu akulu a dziko la South Africa akuunikabe matupi kuti awazindikire.
Komabe, m'modzi mwa anthu ogwira ntchito ku ofesi ya kazembe ku South Africa-ko wauza Zodiak Online kuti ndizovuta kuzindikira anthu chifukwa ena analibe ziphaso zowazindikilitsa komanso ziphaso zoyendera.
(by John-Paul Kayuni-Lilongwe: 10/15/25)
15/10/2025
Barely hours after the Ministry of Foreign Affairs reported that 22 Malawians were involved in a fatal bus accident in South Africa, the Office of the President and Cabinet (OPC) has confirmed that 18 Malawians have been identified among the deceased.
In a statement signed by Secretary to the President and Cabinet, Justin Saidi, the OPC said President Peter Mutharika and First Lady Gertrude Mutharika are “deeply saddened by the tragic accident” and have conveyed their heartfelt condolences to the bereaved families.
Earlier, the Ministry of Foreign Affairs announced that 22 Malawians were on board the ill-fated bus, with 14 confirmed alive and eight reported missing.
The Ministry also stated that 43 people had died in the crash, though it could not immediately confirm whether any of the deceased were Malawian, noting that South African authorities were conducting forensic identification of the victims.
Meanwhile, President Mutharika has reaffirmed his government’s commitment to supporting the bereaved families with all necessary funeral arrangements and extended wishes for a swift recovery to those injured.
(by John-Paul Kayuni-Lilongwe: 10/15/25)
HAPPY MOTHER'S DAY. osaiwala kutipanga follow Odalitsika mulungu amakhalanaye
15/10/2025
Ethel, was born with clubfoot, a condition where her feet curved inward, making it difficult for her to walk, play, or live like other children her age.
For years, she endured the physical and emotional pain of the condition, which followed her into her teenage years.
Her story took a hopeful turn when she crossed paths with Rev. Blessing, a local pastor who had just attended a CURE Malawi training session titled "The Theology of Disability."
The training focused on God’s heart for people with disabilities, challenging harmful beliefs that often associate disability with shame or curse.
When Rev. Blessing met Ethel, he shared what he had learned, that her condition was not a curse, and that children like her are loved by God and filled with purpose.
More than just encouraging words, he informed her that her condition could be corrected through free surgery at Beit CURE International Hospital, Malawi.. Taking it upon himself, the pastor personally accompanied her to the hospital.
Three years later, Ethel’s transformation is undeniable. She now walks with confidence on straightened feet, attends school, helps her family, and lives with a new sense of possibility.
Watch her story: https://vimeo.com/1008454417/1329354ee5?share=copy
15/04/2025
ATULUKA ndipo;-
1) Ma Galimoto owonongeka ndi 9 koma 5 akukonzedwa kale
2) Doc atha kukonza 4 koma alembe kaye kalata ndipo atsate ndondomeko
3) Akatsata ndondomeko atha kumuvomela kapena ayi
Meanwhile, Doc is typing…
Mulungu wakhala ali thandizo lanu kwa nthawi yaitali mwaulele tangolembani amen momuthokoza
13/12/2024
......
Ndizovesa chisoni ndi zolilitsa kuti mulungu wakudzusani ndimoyo koma inu osamuthokoza. Tangonenani AMEN
BOMA NDILOMWELI PALIBE KUSINTHA
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Telephone
Website
Address
LILONGWE TO SALIMA
Lilongwe