Malawi Daily
This Creative Centre is here to educate and inform guardians on different aspects concerning childre
28/12/2024
INE NDI NDANI....? ❤️
28/12/2024
🚨Heartbreak of the year...💔
Basitu woyimba wamkazi, Hezel Mak, angomusiyira mwana kenako mamuna wawuyatsa ulendo, banja latha.
Pepa, Hezel. Heaven is the goal!
Apa walowa gulu lama single mums lachina Miracle Chinga, Tamia Ja…
28/12/2024
Mpangeni tag mwini nkhaniyi
Madeya ayambile panja mpaka nyumba mwanumo Nkhuku ikalowa sekani chitseko,,,mapezedwe a Mpunga tiphunzitsana mawa... Xmas🎅
21/12/2024
Oimbila mpira wamiyendo okwana khumi asanu ndi mmodzi avomelezedwa ngati a FIFA a dziko lino.
Pa oyimbilawa pali Godfrey Nkhakananga, Easter Zimba, Mayamiko Kanjere ndi David Chinoko.
Kumbali ya othandizira ndi Bernadettar Kwimbira, Clemence Kanduku, Pondamali Tembo, Happiness Mbandambanda, Evance Msonda, Lameck Phiri, Samuel Fudzulani, Mphatso Matete ndi Sibusiso Sibande.
Koma kumbali ya oimbila omwe akhoza kumaunika nawo pa kanema (VAR) palibe yemwe watengedwa mdziko muno kamba koti Nkhakananga, Gumbo ndi Tembo onse akanika.
Rose Zimba wakanika kukhala nawo pamndandanda wa FIFA.
Zabwino zonse
21/12/2024
Congratulations to Mighty Mukuru Wanderers FC for being crowned the 2024 Castel Challenge Cup Champions.
21/12/2024
Bad day for the Cities
⚽
20/12/2024
Mozambique ndi chifukwa chimene chimachititsa kuti Tanzania izifuna mbali ina ya Nyanja ya Malawi. Tikuganiza izi chifukwa mbali ina ya nyanjayi ndi ya dziko la Mozambique. Chifukwa choti tinatema kumupatsa neba (Mozambique) naye neba winayu (Tanzania) amafuna titamutemere.
Kumbukirani kuti ngakhale boma la Likoma ndi limodzi mwa maboma a ku Malawi koma bomali limapezeka mbali ya nyanja yomwe ili m'manja mwa Mozambique. Ichi ndi chifukwa chake mzere osonyeza malire a dziko la Malawi ndi Mozambique (international boundary line) umaoneka kuti unadutsa m'nyanja ya Malawi.
Just because he dated u for 4 good years doesn't means he will marry u.
My uncle study medicine for 8 years and he is a DJ now.
Entertainers of the Year— music category winners
Male Secular Artist of the Year
Driemo
Female Secular Artist of the Year
Emmie Deebo
Male Gospel Artist of the Year
Steve Wazisomo Muliya
Female Gospel Artist of the Year
Miracle Chinga
Secular Song of the Year
Kutali by Fadda Motti
13/12/2024
Mutawapeza mungawatani
13/12/2024
Jetu akupuma kuyimba chaka chamawa
Oyimba wachikulire, Jetu adzasiya zoyimbayimbazi chaka chamawa. Dyokhwe, m'modzi mwa adzukulu ake a Jetu, watsimikizira za nkhaniyi.
Iye wanenetsa kuti kaya aMalawi mufune kaya musafune koma Jetu akupumila zoyimbazi chaka cha 2025. Mkufotokoza kwake, wati Agogo akewa akudzapuma kuyimba chifukwa akalamba kwambiri.
Pakadali pano, Jetu yemwe ali ndi zaka 73, watulutsapo nyimbo zingapo zimene zikusangalatsa anthu monga, Wakalamba Wafuna, Chakwaza, Simunatchene imene anayimba ndi m'dzukulu wakeyu ndi zina zambiri. Jetu watulutsaso nyimbo ina yotchedwa 'Waimanya' masiku anayi apitawa imene anthu akuikondaso kwambiri.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Contact the public figure
Telephone
Website
Address
Lilongwe